Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 14:31 - Buku Lopatulika

31 Kapena mfumu yanji pakupita kukomana ndi nkhondo ya mfumu inzake, sayamba wakhala pansi, nafunsana ndi akulu ngati akhoza ndi asilikali ake zikwi khumi kulimbana naye wina uja alikudza kukomana naye ndi asilikali zikwi makumi awiri?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Kapena mfumu yanji pakupita kukomana ndi nkhondo ya mfumu inzake, sathanga wakhala pansi, nafunsana ndi akulu ngati akhoza ndi asilikali ake zikwi khumi kulimbana naye wina uja alikudza kukomana naye ndi asilikali zikwi makumi awiri?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 “Chimodzimodzinso kodi ndi mfumu iti, popita ku nkhondo kukamenyana ndi mfumu ina, siiyamba yakhala pansi nkuganiza bwino? Imaganiziratu ngati ndi asilikali zikwi khumi ingathe kukamenyana ndi mfumu ina ija, imene ikubwera ndi asilikali zikwi makumi aŵiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 “Kapena mfumu imene ikupita ku nkhondo kukamenyana ndi mfumu ina, kodi siyamba yakhala pansi ndi kulingalira ngati ingathe ndi anthu 10,000 kulimbana ndi amene akubwera ndi 20,000?

Onani mutuwo Koperani




Luka 14:31
7 Mawu Ofanana  

Ndipo mfumu ya Israele anayankha, nati, Kamuuzeni, Wakumanga zida asadzikuze ngati wakuvulayo.


Isanjike dzanja lako; ukakumbukira nkhondoyi, sudzateronso.


Uphungu utsimikiza zolingalira, ponya nkhondo utapanga upo.


Usatuluke mwansontho kukalimbana, ungalephere pa kutha kwake, atakuchititsa mnzako manyazi.


ndi kunena kuti, Munthu uyu anayamba kumanga, koma sanathe kumaliza.


Koma ngati sakhoza, atumiza akazembe, pokhala winayo ali kutalitali, nafunsa za mtendere.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa