Luka 14:30 - Buku Lopatulika30 ndi kunena kuti, Munthu uyu anayamba kumanga, koma sanathe kumaliza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 ndi kunena kuti, Munthu uyu anayamba kumanga, koma sanathe kumaliza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Adzati, ‘Mkulu uyu adaayamba kumanga nyumba, koma adalephera kuitsiriza.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 nanena kuti, ‘Munthu uyu anayamba kumanga koma sanathe kutsiriza.’ Onani mutuwo |