Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 14:30 - Buku Lopatulika

30 ndi kunena kuti, Munthu uyu anayamba kumanga, koma sanathe kumaliza.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 ndi kunena kuti, Munthu uyu anayamba kumanga, koma sanathe kumaliza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Adzati, ‘Mkulu uyu adaayamba kumanga nyumba, koma adalephera kuitsiriza.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 nanena kuti, ‘Munthu uyu anayamba kumanga koma sanathe kutsiriza.’

Onani mutuwo Koperani




Luka 14:30
11 Mawu Ofanana  

ndipo inagwa mvula, nidzala mitsinje, ndipo zinaomba mphepo, zinagunda pa nyumbayo; ndipo inagwa; ndi kugwa kwake kunali kwakukulu.


Kuti kungachitike, pamene atakhazika pansi miyala ya kumaziko ake, osakhoza kuimaliza anthu onse akuyang'ana adzayamba kumseka iye,


Kapena mfumu yanji pakupita kukomana ndi nkhondo ya mfumu inzake, sayamba wakhala pansi, nafunsana ndi akulu ngati akhoza ndi asilikali ake zikwi khumi kulimbana naye wina uja alikudza kukomana naye ndi asilikali zikwi makumi awiri?


Koma wolungama wangayo adzakhala ndi moyo wochokera m'chikhulupiriro: Ndipo ngati abwerera, moyo wanga ulibe kukondwera mwa iye.


Koma tikhumba kuti yense wa inu aonetsere changu chomwechi cholinga kuchiyembekezo chokwanira kufikira chitsiriziro;


Mudzipenyerere nokha, kuti mungataye zimene tazichita, koma kuti mulandire mphotho yokwanira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa