Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 14:29 - Buku Lopatulika

29 Kuti kungachitike, pamene atakhazika pansi miyala ya kumaziko ake, osakhoza kuimaliza anthu onse akuyang'ana adzayamba kumseka iye,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Kuti kungachitike, pamene atakhazika pansi miyala ya kumaziko ake, osakhoza kuimaliza anthu onse akuyang'ana adzayamba kumseka iye,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Akapanda kutero, mwina adzaika maziko, nkulephera kuitsiriza. Apo anthu onse, poona zimenezi, adzayamba kumseka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Pakuti ngati ayika maziko ndi kulephera kutsiriza, aliyense amene adzayiona adzamuseka,

Onani mutuwo Koperani




Luka 14:29
4 Mawu Ofanana  

nati, Nanga Iwe, wopasula Kachisi, ndi kummanganso masiku atatu, tadzipulumutsa wekha; ngati uli Mwana wa Mulungu, tatsika pamtandapo.


Pakuti ndani wa inu amene akafuna kumanga nsanja yaitali, sayamba wakhala pansi, nawerengera mtengo wake, aone ngati ali nazo zakuimaliza?


ndi kunena kuti, Munthu uyu anayamba kumanga, koma sanathe kumaliza.


Tavalani zida zonse za Mulungu, kuti mudzakhoze kuchilimika pokana machenjerero a mdierekezi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa