Luka 14:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo mipingo yambiri ya anthu inamuka naye; ndipo Iye anapotoloka, nati kwa iwo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo mipingo yambiri ya anthu inamuka naye; ndipo Iye anapotoloka, nati kwa iwo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Chikhamu cha anthu chinkatsagana ndi Yesu. Tsono Iye adatembenuka naŵauza kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Gulu lalikulu la anthu linkayenda naye Yesu ndipo atatembenukira kwa iwo anati, Onani mutuwo |