Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 14:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo mipingo yambiri ya anthu inamuka naye; ndipo Iye anapotoloka, nati kwa iwo,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo mipingo yambiri ya anthu inamuka naye; ndipo Iye anapotoloka, nati kwa iwo,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Chikhamu cha anthu chinkatsagana ndi Yesu. Tsono Iye adatembenuka naŵauza kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Gulu lalikulu la anthu linkayenda naye Yesu ndipo atatembenukira kwa iwo anati,

Onani mutuwo Koperani




Luka 14:25
4 Mawu Ofanana  

Pomwepo pamene anthu a zikwizikwi a khamu anasonkhana pamodzi, kotero kuti anapondana, Iye anayamba kunena kwa ophunzira ake poyamba, Tachenjerani nokha ndi chotupitsa mikate cha Afarisi, chimene chili chinyengo.


Pakuti ndinena kwa inu, kuti kulibe mmodzi wa amuna oitanidwa aja adzalawa phwando langa.


Munthu akadza kwa Ine, wosada atate wake ndi amake, ndi mkazi wake, ndi ana, ndi abale, ndi alongo ake, inde ndi moyo wake womwe wa iye mwini, sangathe kukhala wophunzira wanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa