Luka 14:24 - Buku Lopatulika24 Pakuti ndinena kwa inu, kuti kulibe mmodzi wa amuna oitanidwa aja adzalawa phwando langa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Pakuti ndinena kwa inu, kuti kulibe mmodzi wa amuna oitanidwa aja adzalawa phwando langa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Kunena zoona, mwa anthu amene ndidaaŵaitana aja palibe ndi mmodzi yemwe amene adzalilaŵe phwando langali.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Ine ndikukuwuzani inu kuti palibe ndi mmodzi yemwe mwa anthu amene anayitanidwa adzalawa phwandolo.’ ” Onani mutuwo |