Luka 14:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo kapoloyo anati, Ambuye, chimene munachilamulira chachitika, ndipo malo atsalapo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo kapoloyo anati, Ambuye, chimene munachilamulira chachitika, ndipo malo atsalapo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Atabwerako wantchito uja adati, ‘Bwana, ndachita zija munandilamulazi, koma malo akalipobe.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 “Wantchitoyo anati, ‘Bwana, zimene munanena zachitika koma malo akanalipobe.’ Onani mutuwo |