Luka 14:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo anati wina, Ine ndakwatira mkazi, ndipo chifukwa chake sindingathe kudza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo anati wina, Ine ndakwatira mkazi, ndipo chifukwa chake sindingathe kudza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Ndipo wina adati, ‘Ndangokwatira tsopano apa, choncho sinditha kubwera.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 “Wina anatinso, ‘Ine ndangokwatira kumene, choncho sinditha kubwera.’ Onani mutuwo |