Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 12:59 - Buku Lopatulika

59 Ine ndinena kwa iwe, Sudzatulukamo konse kufikira utalipira kakobiri kukumaliza.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

59 Ine ndinena kwa iwe, Sudzatulukamo konse kufikira utalipira kakobiri kukumaliza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

59 Ndithu ndikunenetsa kuti sudzatulukamo mpaka utalipira zonse.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

59 Ine ndikuwuzani kuti, simudzatulukamo mpaka mutalipira ndalama zonse.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 12:59
7 Mawu Ofanana  

Ndipo mbuye wake anakwiya, nampereka kwa azunzi, kufikira akambwezere iye mangawa onse.


Pomwepo Iye adzanena kwa iwo a kudzanja lamanzere, Chokani kwa Ine otembereredwa inu, kumoto wa nthawi zonse wokolezedwera mdierekezi ndi angelo ake:


Ndipo amenewa adzachoka kunka ku chilango cha nthawi zonse; koma olungama kumoyo wa nthawi zonse.


Indetu ndinena ndi iwe, sudzatulukamo konse, koma utalipa kakobiri kakumaliza ndiko.


Ndipo anadza mkazi wamasiye waumphawi, ndipo iye anaponyamo tindalama tiwiri tating'ono tokwanira kakobiri kamodzi.


Ndipo pamwamba pa izi, pakati pa ife ndi inu pakhazikika phompho lalikulu, kotero kuti iwo akufuna kuoloka kuchokera kuno kunka kwa inu sangathe, kapena kuchokera kwanuko kuyambuka kudza kwa ife, sangathenso.


Tiziyamika Mulungu nthawi zonse chifukwa cha inu, abale, monga kuyenera; pakuti chikhulupiriro chanu chikula chikulire, ndipo chichulukira chikondano cha inu nonse, yense pa mnzake;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa