Luka 12:59 - Buku Lopatulika59 Ine ndinena kwa iwe, Sudzatulukamo konse kufikira utalipira kakobiri kukumaliza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201459 Ine ndinena kwa iwe, Sudzatulukamo konse kufikira utalipira kakobiri kukumaliza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa59 Ndithu ndikunenetsa kuti sudzatulukamo mpaka utalipira zonse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero59 Ine ndikuwuzani kuti, simudzatulukamo mpaka mutalipira ndalama zonse.” Onani mutuwo |