Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 12:38 - Buku Lopatulika

38 Ndipo akadza ulonda wachiwiri, kapena wachitatu, nakawapeza atero, odala amenewa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 Ndipo akadza ulonda wachiwiri, kapena wachitatu, nakawapeza atero, odala amenewa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 Ngodala antchitowo mbuye waoyo akadzaŵapeza ali choncho pamene iye adzafike, ngakhale pakati pa usiku kapena kuli pafupi kucha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 Zidzakhala bwino kwa antchitowo amene mbuye wawo adzawapeze ali okonzeka, ngakhale iye atabwera pa ora lachiwiri kapena lachitatu usiku.

Onani mutuwo Koperani




Luka 12:38
4 Mawu Ofanana  

Koma dziwani ichi, kuti mwini nyumba akadadziwa nthawi yiti mbala ikudza, iye akadadikira, ndipo sakadalola kuti nyumba yake ibooledwe.


Koma pakati pa usiku panali kufuula, Onani, mkwati! Tulukani kukakomana naye.


Koma zindikirani ichi, kuti mwini nyumba akadadziwa nthawi yake yakudza mbala, akadadikira, ndipo sakadalola nyumba yake ibooledwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa