Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 12:29 - Buku Lopatulika

29 Ndipo inu musafunefune chimene mudzadya, ndi chimene mudzamwa; ndipo musakayike mtima.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Ndipo inu musafunefune chimene mudzadya, ndi chimene mudzamwa; ndipo musakayike mtima.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Nchifukwa chake musamadera nkhaŵa ndi kufunafuna zoti mudye, kapena zoti mumwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Ndipo musayike mtima wanu pa zimene mudzadye kapena kumwa; musade nazo nkhawa.

Onani mutuwo Koperani




Luka 12:29
6 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake musadere nkhawa, ndi kuti, Tidzadya chiyani? Kapena, Tidzamwa chiyani? Kapena, Tidzavala chiyani?


Ndipo Iye anati kwa ophunzira ake, Chifukwa chake ndinena ndinu, Musade nkhawa ndi moyo wanu, chimene mudzadya; kapena ndi thupi lanu, chimene mudzavala.


Kotero ngati simungathe ngakhale chaching'onong'ono, muderanji nkhawa chifukwa cha zina zija?


Pakuti izi zonse mitundu ya anthu a padziko lapansi amazifunafuna; koma Atate wanu adziwa kuti musowa zimenezi.


Ndipo anati kwa iwo, Pamene ndinakutumizani opanda thumba la ndalama, ndi thumba la kamba, ndi nsapato, munasowa kanthu kodi? Anati iwo, Iai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa