Luka 11:50 - Buku Lopatulika50 kuti mwazi wa aneneri onse, wakhetsedwa kuyambira kukhazika kwa dziko lapansi, ukafunidwe kwa anthu a mbadwo uno; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201450 kuti mwazi wa aneneri onse, wakhetsedwa kuyambira kukhazika kwa dziko lapansi, ukafunidwe kwa anthu a mbadwo uno; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa50 Motero anthu amakono adzakhala ndi mlandu chifukwa cha aneneri onse amene adaphedwa chilengedwere dziko lapansi, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero50 Choncho mʼbado uwu udzasenza magazi a aneneri onse amene anakhetsedwa kuyambira pachiyambi cha dziko, Onani mutuwo |