Luka 11:48 - Buku Lopatulika48 Chomwecho muli mboni, ndipo muvomera ntchito za makolo anu; chifukwa iwotu anawapha, koma inu muwamangira iwo zapamanda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 Chomwecho muli mboni, ndipo muvomera ntchito za makolo anu; chifukwa iwotu anawapha, koma inu muwamangira iwo zapamanda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 Apo mukutsimikiza kuti mukuvomereza ntchito za makolo anuwo, popeza kuti iwowo adapha aneneriwo, inuyo nkumamanga ziliza zao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 Tsono potero mumachitira umboni za zimene makolo anu anachita. Anapha aneneri, ndipo inu mumawaka manda awo. Onani mutuwo |