Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 11:38 - Buku Lopatulika

38 Ndipo anazizwa Mfarisiyo, pakuona kuti anayamba chakudya asanasambe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 Ndipo anazizwa Mfarisiyo, pakuona kuti anayamba chakudya asanasambe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 Mfarisiyo adadabwa poona kuti Yesu wayamba kudya osatsata mwambo wao wa kasambidwe ka m'manja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 Mfarisiyo anadabwa atazindikira kuti Yesu anayamba kudya wosatsata mwambo wawo wakasambidwe ka mʼmanja.

Onani mutuwo Koperani




Luka 11:38
5 Mawu Ofanana  

Ndipo pakumva ichi, Yesu anazizwa, nati kwa iwo akumtsata, Indetu ndinena kwa inu, ngakhale mwa Israele, sindinapeze chikhulupiriro chotere.


Ndipo pakulankhula Iye, anamuitana Mfarisi kuti adye naye; ndipo analowa naseama kudya.


Pamenepo padauka kufunsana mwa ophunzira ake a Yohane ndi Myuda za mayeretsedwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa