Luka 11:37 - Buku Lopatulika37 Ndipo pakulankhula Iye, anamuitana Mfarisi kuti adye naye; ndipo analowa naseama kudya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndipo pakulankhula Iye, anamuitana Mfarisi kuti adye naye; ndipo analowa naseama kudya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Pamene Yesu adatsiriza kulankhula, wina wa m'gulu la Afarisi adamuitana kuti akadye naye. Tsono Yesu adaloŵa m'nyumba nakakhala podyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Yesu atamaliza kuyankhula, Mfarisi wina anamuyitana kuti akadye naye. Tsono Yesu analowa mʼnyumba ndi kukhala podyera. Onani mutuwo |