Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 11:35 - Buku Lopatulika

35 Potero yang'anira kuunika kuli mwa iwe kungakhale mdima.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

35 Potero yang'anira kuunika kuli mwa iwe kungakhale mdima.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

35 Chenjera tsono kuti kuŵala kumene kuli mwa iwe kusasanduke mdima.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

35 Onetsetsani tsono, kuti kuwunika kuli mwa inu si mdima.

Onani mutuwo Koperani




Luka 11:35
17 Mawu Ofanana  

Ilipo njira yooneka kwa mwamuna ngati yoongoka, koma matsiriziro ake ndi njira za imfa.


Kodi uona munthu wodziyesa wanzeru? Ngakhale chitsiru chidzachenjera koma ameneyo ai.


Diso ndilo nyali ya thupi; chifukwa chake ngati diso lako lili la kumodzi, thupi lako lonse lidzakhala lowalitsidwa.


Nyali ya thupi ndiyo diso lako; pamene paliponse diso lako lili langwiro thupi lako lonse liunikidwanso monsemo; koma likakhala loipa, thupi lako lomwe lili la mdima wokhawokha.


Pamenepo, ngati thupi lako lonse liunikidwa losakhala nalo dera lake lamdima, lidzakhala lounikidwa monsemo, ngati pamene nyali ndi kuwala kwake ikuunikira iwe.


Pakunena kuti ali anzeru, anapusa;


Pakuti iye wakusowa izi ali wakhungu, wa chimbuuzi, woiwala matsukidwe ake potaya zoipa zake zakale.


Pakuti polankhula mau otukumuka opanda pake, anyengerera pa zilakolako za thupi, ndi zonyansa, anthu amene adayamba kupulumuka kwa iwo a mayendedwe olakwa;


Chifukwa unena kuti ine ndine wolemera, ndipo chuma ndili nacho, osasowa kanthu; ndipo sudziwa kuti ndiwe watsoka, ndi wochititsa chifundo, ndi wosauka, ndi wakhungu, ndi wausiwa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa