Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 11:33 - Buku Lopatulika

33 Palibe munthu, atayatsa nyali, aiika m'chipinda chapansi, kapena pansi pa mbiya, koma pa choikapo chake, kuti iwo akulowamo aone kuunika.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Palibe munthu, atayatsa nyali, aiika m'chipinda chapansi, kapena pansi pa mbiya, koma pa choikapo chake, kuti iwo akulowamo aone kuunika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 “Munthu sati akayatsa nyale, nkuiika m'chipinda chapansi kapena kuivundikira ndi mbiya. Koma amaiika pa malo oonekera, kuti anthu oloŵa m'nyumbamo aone kuŵala kwake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 “Palibe amene amayatsa nyale ndi kuyiika pa malo poti sionekera, kapena pansi pa mtsuko. Mʼmalo mwake amayika pa choyikapo chake, kuti iwo amene akulowamo aone kuwunika.

Onani mutuwo Koperani




Luka 11:33
7 Mawu Ofanana  

Chimene ndikuuzani inu mumdima, tachinenani poyera; ndi chimene muchimva m'khutu, muchilalikire pa matsindwi a nyumba.


Yesu anayankha, Kodi sikuli maora khumi ndi awiri usana? Ngati munthu ayenda usana sakhumudwa, chifukwa apenya kuunika kwa dziko lino lapansi.


Ndadza Ine kuunika kudziko lapansi, kuti yense wokhulupirira Ine asakhale mumdima.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa