Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 11:28 - Buku Lopatulika

28 Koma Iye anati, Inde, koma odala iwo akumva mau a Mulungu, nawasunga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Koma Iye anati, Inde, koma odala iwo akumva mau a Mulungu, nawasunga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Koma Yesu adati, “Iyai, odala ndi anthu amene amamva mau a Mulungu naŵagwiritsa ntchito.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Koma Yesu anayankha kuti, “Odala ndi amene amamva mawu a Mulungu ndi kuwasunga.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 11:28
16 Mawu Ofanana  

Aleluya. Wodala munthu wakuopa Yehova, wakukondwera kwambiri ndi malamulo ake.


Wodala yense wakuopa Yehova, wakuyenda m'njira zake.


Wosunga lamulo asunga moyo wake; wonyalanyaza mayendedwe ake adzafa.


Ndipo tsopano, ananga, mundimvere ine, ngodala akusunga njira zanga.


Koma Iye anayankha, nati kwa iwo, Amai wanga ndi abale anga ndiwo amene akumva mau a Mulungu, nawachita.


Ngati mudziwa izi, odala inu ngati muzichita.


Wodala iye amene awerenga, ndi iwo amene akumva mau a chinenerocho, nasunga zolembedwa momwemo; pakuti nthawi yayandikira.


Odala iwo amene atsuka miinjiro yao, kuti akakhale nao ulamuliro pa mtengo wa moyo, ndi kuti akalowe m'mzinda pazipata.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa