Luka 11:28 - Buku Lopatulika28 Koma Iye anati, Inde, koma odala iwo akumva mau a Mulungu, nawasunga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Koma Iye anati, Inde, koma odala iwo akumva mau a Mulungu, nawasunga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Koma Yesu adati, “Iyai, odala ndi anthu amene amamva mau a Mulungu naŵagwiritsa ntchito.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Koma Yesu anayankha kuti, “Odala ndi amene amamva mawu a Mulungu ndi kuwasunga.” Onani mutuwo |