Levitiko 9:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo Aroni anaweyula ngangazo ndi mwendo wathako wa ku dzanja lamanja zikhale nsembe yoweyula pamaso pa Yehova; monga Iye anauza Mose. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo Aroni anaweyula ngangazo ndi mwendo wathako wa ku dzanja lamanja zikhale nsembe yoweyula pamaso pa Yehova; monga Iye anauza Mose. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Koma Aroni adaweyula ngangazo ndi ntchafu ya ku dzanja lamanja, kuti zikhale chopereka choweyula pamaso pa Chauta, monga momwe Mose adaalamulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Koma zidale ndi ntchafu ya kumanja Aaroni anaziweyula ngati chopereka choweyula pamaso pa Yehova. Onani mutuwo |