Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 9:20 - Buku Lopatulika

20 ndipo anaika mafuta pa ngangazo, natentha mafutawo paguwa la nsembe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 ndipo anaika mafuta pa ngangazo, natentha mafutawo pa guwa la nsembe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Anawo adaika mafuta pa nganga, ndipo Aroni adatentha mafutawo pa guwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Ana a Aaroni anayika mafutawo pa zidale. Pambuyo pake Aaroni anatentha mafutawo pa guwa lansembe.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 9:20
4 Mawu Ofanana  

ndi mafuta a ng'ombe; ndi a nkhosa yamphongoyo, ndi mchira wamafuta, ndi chophimba matumbo, ndi impso, ndi chokuta cha mphafa;


Ndipo Aroni anaweyula ngangazo ndi mwendo wathako wa ku dzanja lamanja zikhale nsembe yoweyula pamaso pa Yehova; monga Iye anauza Mose.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa