Levitiko 9:18 - Buku Lopatulika18 Anaphanso ng'ombe, ndi nkhosa yamphongoyo, ndizo nsembe zoyamika za anthu; ndi ana a Aroni anapereka kwa iye mwaziwo, ndipo anauwaza paguwa la nsembe pozungulira, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Anaphanso ng'ombe, ndi nkhosa yamphongoyo, ndizo nsembe zoyamika za anthu; ndi ana a Aroni anapereka kwa iye mwaziwo, ndipo anauwaza pa guwa la nsembe pozungulira, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Tsono adaphanso ng'ombe ndi nkhosa yamphongo, kuperekera anthu nsembe yachiyanjano. Pambuyo pake ana a Aroni adampatsira magazi, ndipo iye adathira magaziwo pa guwa molizungulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Tsono Aaroni anapha ngʼombe ndi nkhosa yayimuna monga nsembe yachiyanjano ya anthu. Ana ake anamupatsira magazi ndipo anawawaza mbali zonse za guwa. Onani mutuwo |