Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 9:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo anapereka nsembe yopsereza kwa iye, chiwalochiwalo, ndi mutu wake; ndipo anazitentha paguwa la nsembe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo anapereka nsembe yopsereza kwa iye, chiwalochiwalo, ndi mutu wake; ndipo anazitentha pa guwa la nsembe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Pambuyo pake adampatsira nyama ya nsembe yopsereza yoduladula, pamodzi ndi mutu wake womwe, ndipo iye adazitentha pa guwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Ana akewo anamupatsa nyama yoduladula ya nsembe yopsereza ija pamodzi ndi mutu ndipo anazitentha pa guwa.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 9:13
4 Mawu Ofanana  

nang'ambe mapiko ake osawachotsa konse ai; ndipo wansembeyo aitenthe paguwa la nsembe, pa nkhuni zili pamoto; ndiyo nsembe yopsereza, nsembe yamoto, ya fungo lokoma la kwa Yehova.


ndi ana a Aroni, ansembewo, akonze ziwalozo, mutu, ndi mafuta pa nkhuni zili pa moto wa paguwa la nsembe;


Ndipo anapha nsembe yopsereza; ndi ana a Aroni anapereka mwaziwo kwa iye, ndipo anauwaza paguwa la nsembe pozungulira.


Ndipo anatsuka matumbo ndi miyendo, nazitentha pa nsembe yopsereza paguwa la nsembe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa