Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 9:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo anapha nsembe yopsereza; ndi ana a Aroni anapereka mwaziwo kwa iye, ndipo anauwaza paguwa la nsembe pozungulira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo anapha nsembe yopsereza; ndi ana a Aroni anapereka mwaziwo kwa iye, ndipo anauwaza pa guwa la nsembe pozungulira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Tsono adapha nyama ya nsembe yopsereza, ndipo ana ake a Aroniyo atampatsira magazi, iye adawaza magaziwo pa guwa molizungulira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Kenaka anapha nsembe yopsereza. Ana a Aaroni atabwera ndi magazi kwa iye, Aaroniyo anawawaza mbali zonse za guwa.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 9:12
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Aroni analankhula ndi Mose, nati, Taonani, lero abwera nayo nsembe yao yauchimo ndi nsembe yao yopsereza pamaso pa Yehova; ndipo zandigwera zotere; ndikadadya nsembe yauchimo lero, kukadakomera kodi pamaso pa Yehova?


Ndipo anatentha ndi moto nyamayi ndi chikopa kunja kwa chigono.


Ndipo anapereka nsembe yopsereza kwa iye, chiwalochiwalo, ndi mutu wake; ndipo anazitentha paguwa la nsembe.


Ndipo anabwera nayo nsembe yopsereza naipereka monga mwa lemba lake.


Ndipo ana a Aroni anasendera nao mwazi kwa iye; ndipo anaviika chala chake m'mwazimo naupaka pa nyanga za guwa la nsembe, nathira mwaziwo patsinde paguwa la nsembe;


ndipo yendani m'chikondi monganso Khristu anakukondani inu, nadzipereka yekha m'malo mwathu, chopereka ndi nsembe kwa Mulungu, ikhale fungo lonunkhira bwino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa