Levitiko 9:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo anatentha ndi moto nyamayi ndi chikopa kunja kwa chigono. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo anatentha ndi moto nyamayi ndi chikopa kunja kwa chigono. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Nyama yake ndi chikopa chake, adazitenthera kunja kwake kwa mahema. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Koma nyama ndi chikopa anazitenthera kunja kwa msasa. Onani mutuwo |