Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 9:11 - Buku Lopatulika

11 Ndipo anatentha ndi moto nyamayi ndi chikopa kunja kwa chigono.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo anatentha ndi moto nyamayi ndi chikopa kunja kwa chigono.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Nyama yake ndi chikopa chake, adazitenthera kunja kwake kwa mahema.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Koma nyama ndi chikopa anazitenthera kunja kwa msasa.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 9:11
7 Mawu Ofanana  

Ndipo atulutse ng'ombeyo kunja kwa chigono, ndi kuitentha monga anatenthera ng'ombe yoyamba ija; ndiyo nsembe yauchimo ya kwa msonkhano.


Koma ng'ombeyo, ndi chikopa chake, ndi nyama yake, ndi chipwidza chake, anazitentha ndi moto kunja kwa chigono; monga Yehova adamuuza Mose.


koma mafutawo, ndi impso, ndi chokuta cha mphafa za nsembe yauchimo, anazitentha paguwa la nsembe; monga Yehova analamula Mose.


Ndipo anapha nsembe yopsereza; ndi ana a Aroni anapereka mwaziwo kwa iye, ndipo anauwaza paguwa la nsembe pozungulira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa