Levitiko 8:34 - Buku Lopatulika34 Monga anachita lero lino, momwemo Yehova analamula kuchita, kukuchitirani chotetezera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Monga anachita lero lino, momwemo Yehova anauza kuchita, kukuchitirani chotetezera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Chauta adatilamula kuti tikuchiteni zimene takuchitanizi, kuti ukhale mwambo wopepesera machimo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Zimene zachitika lerozi analamula ndi Yehova kuti zichitike ngati nsembe yopepesera machimo anu. Onani mutuwo |