Levitiko 8:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo anatenga mafutawo ndi mchira wamafuta, ndi mafuta onse a pamatumbo, ndi chokuta cha mphafa, ndi impso ziwiri, ndi mafuta ake, ndi mwendo wathako wa ku dzanja lamanja; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo anatenga mafutawo ndi mchira wamafuta, ndi mafuta onse a pamatumbo, ndi chokuta cha mphafa, ndi impso ziwiri, ndi mafuta ake, ndi mwendo wathako wa ku dzanja lamanja; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Adatenga mafuta, mchira wamafuta, mafuta onse akumatumbo, mphumphu ya mafuta akuchiŵindi, imso ziŵiri ndi mafuta ake omwe, ndi ntchafu ya ku dzanja lamanja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Anatenganso mafuta ake, mafuta a ku mchira wake, mafuta okuta matumbo, mafuta okuta chiwindi, impsyo zonse ziwiri ndi mafuta ake ndiponso ntchafu yakumanja. Onani mutuwo |