Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 8:20 - Buku Lopatulika

20 Ndipo anapadzula mphongoyo ziwalo zake; ndi Mose anatentha mutuwo ndi ziwalo, ndi mafuta.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Ndipo anapadzula mphongoyo ziwalo zake; ndi Mose anatentha mutuwo ndi ziwalo, ndi mafuta.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Atadula nkhosayo nthulinthuli, Mose adatentha mutu wake ndi nthuli zija ndi mafuta ake omwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Anayidula nkhosayo nthulinthuli ndipo anatentha mutu wake, nthulizo ndi mafuta.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 8:20
3 Mawu Ofanana  

Ndi zichiri zangowe, chikhato m'litali mwake, zinamangika m'katimo pozungulirapo; ndi pamagome panali nyama ya nsembe.


ndi ana a Aroni, ansembewo, akonze ziwalozo, mutu, ndi mafuta pa nkhuni zili pa moto wa paguwa la nsembe;


Ndipo anaipha; ndi Mose anawaza mwazi wake paguwa la nsembe pozungulira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa