Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 8:19 - Buku Lopatulika

19 Ndipo anaipha; ndi Mose anawaza mwazi wake paguwa la nsembe pozungulira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ndipo anaipha; ndi Mose anawaza mwazi wake pa guwa la nsembe pozungulira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Kenaka Mose adaipha nathira magazi ake pa guwa mozungulira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Ndipo Mose anapha nkhosayo ndi kuwaza magazi ake mbali zonse zaguwalo.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 8:19
5 Mawu Ofanana  

Momwemo anapha ng'ombezo, ndi ansembe analandira mwazi, nauwaza paguwa la nsembe, napha nkhosa zamphongozo, nawaza mwazi paguwa la nsembe; anaphanso anaankhosa aja, nawaza mwazi paguwa la nsembe.


Ndipo aiphere iyo pa mbali ya kumpoto ya guwa la nsembe, pamaso pa Yehova; ndipo ana a Aroni, ansembewo, awaze mwazi wake paguwa la nsembe pozungulira.


Ndipo anabwera nayo nkhosa yamphongo ya nsembe yopsereza; ndipo Aroni ndi ana ake aamuna anaika manja ao pamutu pa mphongoyo.


Ndipo anapadzula mphongoyo ziwalo zake; ndi Mose anatentha mutuwo ndi ziwalo, ndi mafuta.


Ndiponso chihema ndi zotengera zonse za utumikiro anaziwaza momwemo ndi mwaziwo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa