Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 8:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo anabwera nayo nkhosa yamphongo ya nsembe yopsereza; ndipo Aroni ndi ana ake aamuna anaika manja ao pamutu pa mphongoyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo anabwera nayo nkhosa yamphongo ya nsembe yopsereza; ndipo Aroni ndi ana ake amuna anaika manja ao pamutu pa mphongoyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Pambuyo pake adapereka nkhosa yamphongo ya nsembe yopsereza, ndipo Aroni ndi ana ake adasanjika manja ao pamutu pa nkhosayo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Kenaka anabwera ndi nkhosa yayimuna ya nsembe yopsereza, ndipo Aaroni ndi ana ake aamuna anasanjika manja awo pamutu pake.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 8:18
6 Mawu Ofanana  

Ndipo akulu a khamulo aike manja ao pamutu pa ng'ombeyo, pamaso pa Yehova; naiphe ng'ombeyo pamaso pa Yehova.


Ndipo anaipha; ndi Mose anawaza mwazi wake paguwa la nsembe pozungulira.


Tenga Aroni ndi ana ake pamodzi naye ndi zovalazo, ndi mafuta odzozawo; ndi ng'ombe ya nsembe yauchimoyo, ndi nkhosa zamphongo ziwirizo, ndi dengu la mkate wopanda chotupitsawo;


Ndipo anabwera nayo nsembe yopsereza naipereka monga mwa lemba lake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa