Levitiko 8:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo anatsanulirako mafuta odzoza pamutu pa Aroni, namdzoza kumpatula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo anatsanulirako mafuta odzoza pamutu pa Aroni, namdzoza kumpatula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Mafuta ena odzozerawo adaŵathira pamutu pa Aroni, namdzoza, ndi kumsandutsa wopatulika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Anathira mafuta wodzozera ena pamutu pa Aaroni ndipo anamudzoza ndi kumupatula. Onani mutuwo |