Levitiko 7:32 - Buku Lopatulika32 Ndipo mwendo wathako wa ku dzanja lamanja muupereke kwa wansembe ukhale nsembe yokweza yochokera ku nsembe zoyamika zanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ndipo mwendo wathako wa ku dzanja lamanja muupereke kwa wansembe ukhale nsembe yokweza yochokera ku nsembe zoyamika zanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Wansembe mumpatsenso ntchafu ya ku dzanja lamanja, kuti ikhale chopereka cha pa nsembe yanu yachiyanjano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Mumupatse wansembe ntchafu ya kumanja ya nsembe yanu yachiyanjano kuti ikhale chopereka chanu kwa iye. Onani mutuwo |