Levitiko 7:31 - Buku Lopatulika31 Ndipo wansembeyo atenthe mafutawo paguwa la nsembe; koma ngangayo ikhale ya Aroni ndi ana ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ndipo wansembeyo atenthe mafutawo pa guwa la nsembe; koma ngangayo ikhale ya Aroni ndi ana ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Apo wansembe atenthe mafuta pa guwa, koma ngangayo ikhale ya Aroni ndi ana ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Wansembe atenthe mafutawo pa guwa koma chidalecho chikhale cha Aaroni ndi ana ake. Onani mutuwo |