Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 7:29 - Buku Lopatulika

29 Lankhula ndi ana a Israele, ndi kuti, Wakubwera nayo nsembe yoyamika yake kwa Yehova, azidza nacho chopereka chake kwa Yehova chochokera ku nsembe yoyamika yake;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Lankhula ndi ana a Israele, ndi kuti, Wakubwera nayo nsembe yoyamika yake kwa Yehova, azidza nacho chopereka chake kwa Yehova chochokera ku nsembe yoyamika yake;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 “Uza Aisraele kuti, ‘Munthu amene apereka nsembe yake yachiyanjano kwa Chauta, abwere ndi gawo la nsembeyo kwa Chauta. Pa nsembe yake yachiyanjanoyo

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 “Awuze Aisraeli kuti, Aliyense amene apereka nsembe yachiyanjano kwa Yehova, abwere ndi gawo la nsembeyo kwa Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 7:29
7 Mawu Ofanana  

Ndipo chilamulo cha nsembe zoyamika, zimene azibwera nazo kwa Yehova ndi ichi:


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,


ndipo anaika mafuta pa ngangazo, natentha mafutawo paguwa la nsembe.


mwa Iyenso kuyanjanitsa zinthu zonse kwa Iye mwini, atachita mtendere mwa mwazi wa mtanda wake; mwa Iyetu, kapena za padziko, kapena za mu Mwamba.


koma ngati tiyenda m'kuunika, monga Iye ali m'kuunika, tiyanjana wina ndi mnzake, ndipo mwazi wa Yesu Mwana wake utisambitsa kutichotsera uchimo wonse.


Ndipo machitidwe a ansembe akuchitira anthu ndiwo, kuti pamene munthu aliyense akapereka nsembe, mnyamata wa wansembeyo akabwera, nyama ili chiwirire, ndi chovuulira cha ngowe cha mano atatu m'dzanja lake;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa