Levitiko 7:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo musamadya mwazi uliwonse, kapena wa mbalame, kapena wa nyama, m'nyumba zanu zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo musamadya mwazi uliwonse, kapena wa mbalame, kapena wa nyama, m'nyumba zanu zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Ndiponso kulikonse kumene akakhale, asadye magazi aliwonse, ambalame kapena anyama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Ndipo kulikonse kumene mukakhale musakadye magazi a mbalame iliyonse kapena magazi a nyama iliyonse. Onani mutuwo |