Levitiko 7:23 - Buku Lopatulika23 Lankhula ndi ana a Israele ndi kuti, Musamadya mafuta ali onse, a ng'ombe, kapena a nkhosa, kapena a mbuzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Lankhula ndi ana a Israele ndi kuti, Musamadya mafuta ali onse, a ng'ombe, kapena a nkhosa, kapena a mbuzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 “Uza Aisraele kuti asadye mafuta ang'ombe, kapena ankhosa kapenanso ambuzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 “Awuze Aisraeli kuti, ‘Musadye mafuta a ngʼombe, nkhosa kapenanso mbuzi. Onani mutuwo |