Levitiko 7:20 - Buku Lopatulika20 Koma munthu akadya nyama ya nsembe zoyamika za Yehova, pokhala nacho chomdetsa, munthuyo achotsedwe kwa anthu a mtundu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Koma munthu akadya nyama ya nsembe zoyamika za Yehova, pokhala nacho chomdetsa, munthuyo asadzidwe kwa anthu a mtundu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Koma munthu woipitsidwa akadya nyama ya nsembe yachiyanjano yopereka kwa Chauta, achotsedwe pakati pa Aisraele anzake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Koma ngati munthu wina amene ndi wosayeretsedwa adya nyama ya nsembe yachiyanjano imene ndi ya Yehova, ameneyo achotsedwe pakati pa anthu a mtundu wake. Onani mutuwo |