Levitiko 6:7 - Buku Lopatulika7 ndipo wansembeyo amchitire chomtetezera pamaso pa Yehova, ndipo adzakhululukidwa; kunena zilizonse akazichita ndi kupalamula nazo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 ndipo wansembeyo amchitire chomtetezera pamaso pa Yehova, ndipo adzakhululukidwa; kunena zilizonse akazichita ndi kupalamula nazo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono wansembe achite mwambo wopepesera machimo a munthuyo pamaso pa Chauta, ndipo zonse zimene wochimwayo adachita napalamula pakutero, zidzakhululukidwa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Kenaka wansembe achite mwambo wopepesera tchimo la munthuyo pamaso pa Yehova, ndipo adzakhululukidwa chilichonse chomwe anachita kuti akhale wopalamula.” Onani mutuwo |