Levitiko 6:5 - Buku Lopatulika5 kapena chilichonse analumbirapo monama; achibwezere chonsechi, naonjezepo, limodzi la magawo asanu; apereke ichi kwa mwini wake tsiku lotsutsidwa iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 kapena chilichonse analumbirapo monama; achibwezere chonsechi, naonjezepo, limodzi la magawo asanu; apereke ichi kwa mwini wake tsiku lotsutsidwa iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pa tsiku limene apezeke kuti wapalamuladi, abweze zonsezo ndi kuwonjezapo chimodzi mwa zigawo zisanu zilizonse, tsono amubwezere mwini wakeyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 kapena zimene analumbira monyengazo. Pa tsiku limene apezeke kuti wapalamuladi, iye ayenera kumubwezera mwini wake zinthu zonsezi ndi kuwonjezerapo chimodzi mwa zigawo zisanu zilizonse. Onani mutuwo |
Ndikalipo ine; chitani umboni wonditsutsa pamaso pa Yehova, ndi pamaso pa wodzozedwa wake; ndinalanda ng'ombe ya yani? Kapena ndinalanda bulu wa yani? Ndinanyenga yani? Ndinasutsa yani? Ndinalandira m'manja mwa yani chokometsera mlandu kutseka nacho maso anga? Ngati ndinatero ndidzachibwezera kwa inu.