Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 6:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo zopereka zaufa zonse za wansembe azitenthe konse; asamazidya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo zopereka zaufa zonse za wansembe azitenthe konse; asamazidya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Chopereka cha chakudya chilichonse cha wansembe chikhale chopsereza kwathunthu, asachidye ai.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Nsembe iliyonse yachakudya ya wansembe izitenthedwa kwathunthu, isamadyedwe.”

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 6:23
8 Mawu Ofanana  

Koma ng'ombe ya nsembe yauchimo, ndi mbuzi ya nsembe yauchimo, zimene mwazi wao analowa nao kuchita nao chotetezera m'malo opatulika, atuluke nazo kunja kwa chigono; natenthe ndi moto zikopa zao, ndi nyama zao, ndi chipwidza chao.


Ndipo chotsalira cha nsembe yaufa chikhale cha Aroni ndi ana ake; ndicho chopatulika kwambiri cha nsembe zamoto za Yehova.


inde ng'ombe yonse, kunja kwa chigono, kunka nayo kumalo koyera, kumene atayako mapulusa, naitenthe pankhuni ndi moto; aitenthe potayira mapulusa.


Ndipo atulutse ng'ombeyo kunja kwa chigono, ndi kuitentha monga anatenthera ng'ombe yoyamba ija; ndiyo nsembe yauchimo ya kwa msonkhano.


Ndipo wansembe wodzozedwayo atengeko mwazi wa ng'ombeyo, nabwere nao ku chihema chokomanako;


Ndipo wansembe wodzozedwa m'malo mwake, wa mwa ana ake, achite ichi; likhale lemba losatha; achitenthe konse kwa Yehova.


Ndipo Yehova analankhula ndi Mose, nati,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa