Levitiko 6:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo chotsalira chake adye Aroni ndi ana ake; achidye chopanda chotupitsa m'malo opatulika; pa bwalo la chihema chokomanako achidye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo chotsalira chake adye Aroni ndi ana ake; achidye chopanda chotupitsa m'malo opatulika; pa bwalo la chihema chokomanako achidye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Tsono Aroni ndi ana ake adye zimene zatsalapo. Zikhale zosafufumitsa, ndipo azidyere pa malo oyera, ndiye kuti pa bwalo la chihema chamsonkhano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Aaroni ndi ana ake azidya zimene zatsala koma azidya zopanda yisiti ku malo wopatulika, ku bwalo la tenti ya msonkhano. Onani mutuwo |