Levitiko 6:11 - Buku Lopatulika11 Pamenepo avule zovala zake, navale zovala zina, nachotse phulusa kunka nalo kunja kwa chigono, kumalo koyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Pamenepo avule zovala zake, navale zovala zina, nachotse phulusa kunka nalo kunja kwa chigono, kumalo koyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono avule zovala zake, avale zina, ndipo aole phulusalo nkukaliika pa malo oyeretsedwa kunja kwa mahema. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Akatero avule zovala zakezo ndi kuvala zovala zina. Kenaka atulutse phulusalo ndi kukaliyika pa malo woyeretsedwa kunja kwa chithando. Onani mutuwo |