Levitiko 5:19 - Buku Lopatulika19 Iyo ndiyo nsembe yopalamula; munthuyu anapalamula ndithu pamaso pa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Iyo ndiyo nsembe yopalamula; munthuyu anapalamula ndithu pamaso pa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Imeneyo ndiyo nsembe yopepesera kupalamula, chifukwa munthuyo ndi wopalamula pamaso pa Chauta.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Imeneyi ndi nsembe yopepesera kupalamula popeza munthuyo wapezeka wolakwa pamaso pa Yehova.” Onani mutuwo |