Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 5:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Chauta adauza Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Yehova anawuza Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 5:14
4 Mawu Ofanana  

Ndipo wansembe amchitire chomtetezera chifukwa cha kuchimwa kwake adachimwira chimodzi cha izi, ndipo adzakhululukidwa; ndipo chotsalira chikhale cha wansembe, monga umo amachitira chopereka chaufacho.


Munthu akachita mosakhulupirika, nakachimwa osati dala, pa zopatulika za Yehova, azidza nayo nsembe yake yopalamula kwa Yehova, ndiyo nkhosa yamphongo yopanda chilema, ya m'gulu lake, monga umayesa mtengo wake potchula masekeli a siliva, kunena sekeli wa malo opatulika, ikhale nsembe yopalamula;


Ndipo chilamulo cha nsembe yopalamula ndi ichi: ndiyo yopatulika kwambiri.


Nena ndi ana a Israele, ndi kuti Mwamuna kapena mkazi akachita tchimo lililonse amachita anthu, kuchita mosakhulupirika pa Yehova, nakapalamuladi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa