Levitiko 4:34 - Buku Lopatulika34 Ndipo wansembe atengeko mwazi wa nsembe yauchimo ndi chala chake, nauike pa nyanga za guwa la nsembe yopsereza, ndi kuthira mwazi wake wonse patsinde pa guwa la nsembe; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndipo wansembe atengeko mwazi wa nsembe yauchimo ndi chala chake, nauike pa nyanga za guwa la nsembe yopsereza, ndi kuthira mwazi wake wonse patsinde pa guwa la nsembe; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Pambuyo pake wansembe atengeko magazi a nkhosayo ndi chala chake, ndipo aŵapake pa nyanga za guwa la nsembe zopsereza, ndi kuthira magazi otsalawo patsinde pa guwalo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Kenaka wansembe atengeko ndi chala chake magazi a mwana wankhosa uja ndi kuwapaka pa nyanga za guwa lansembe zopsereza. Magazi otsalawo athire pa tsinde la guwalo. Onani mutuwo |