Levitiko 4:32 - Buku Lopatulika32 Ndipo akadza nayo nkhosa, ndiyo chopereka chake, ikhale nsembe yauchimo, azidza nayo yaikazi, yopanda chilema. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ndipo akadza nayo nkhosa, ndiyo chopereka chake, ikhale nsembe yauchimo, azidza nayo yaikazi, yopanda chilema. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 “Ngati munthu abwera kudzapereka nkhosa ya nsembe yopepesera machimo, nkhosa yake ikhale yaikazi, yopanda chilema. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 “ ‘Ngati munthu apereka mwana wankhosa ngati chopereka chopepesera tchimo lake, abwere ndi mwana wankhosa wamkazi wopanda chilema. Onani mutuwo |