Levitiko 4:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo atenthe mafuta ake onse paguwa la nsembe, monga mafuta a nsembe yoyamika; ndipo wansembe amchitire chomtetezera, ndipo adzakhululukidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo atenthe mafuta ake onse pa guwa la nsembe, monga mafuta a nsembe yoyamika; ndipo wansembe amchitire chomtetezera, ndipo adzakhululukidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Kenaka mafuta ake onse aŵatenthere pa guwa, monga momwe amachitira ndi mafuta a nsembe yachiyanjano. Wansembeyo atachita mwambo wopepesera machimo a wopalamula uja, munthuyo adzakhululukidwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Wansembeyo atenthe mafuta onse pa guwapo monga amatenthera chopereka chachiyanjano. Pochita zimenezi, wansembe adzapereka nsembe yopepesera tchimo la munthuyo, ndipo adzakhululukidwa. Onani mutuwo |