Levitiko 4:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo achotse mafuta ake onse, nawatenthe paguwa la nsembe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo achotse mafuta ake onse, nawatenthe pa guwa la nsembe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Kenaka mafuta ake onse aŵachotse ndi kuŵatenthera pa guwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Kenaka achotse mafuta onse a ngʼombeyo ndi kuwatentha pa guwa, Onani mutuwo |