Levitiko 4:18 - Buku Lopatulika18 Naike mwazi wina pa nyanga za guwa la nsembe, lokhala pamaso pa Yehova, lokhala m'chihema chokomanako; nathire mwazi wonse patsinde pa guwa la nsembe yopsereza, lokhala pa khomo la chihema chokomanako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Naike mwazi wina pa nyanga za guwa la nsembe, lokhala pamaso pa Yehova, lokhala m'chihema chokomanako; nathire mwazi wonse patsinde pa guwa la nsembe yopsereza, lokhala pa khomo la chihema chokomanako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Pambuyo pake magaziwo aŵapake pa nyanga za guwa limene lili m'chihema chamsonkhano pamaso pa Chauta. Magazi ena otsala aŵathire patsinde pa guwa la nsembe zopsereza, limene lili pa khomo la chihema chamsonkhano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Pambuyo pake iye apake magaziwo pa nyanga za guwa limene lili pamaso pa Yehova mu tenti ya msonkhano. Magazi ena otsalawo awathire pa tsinde pa guwa lansembe zopsereza limene lili pa khomo la tenti ya msonkhano. Onani mutuwo |