Levitiko 27:7 - Buku Lopatulika7 Akakhala munthu wa zaka makumi asanu ndi limodzi ndi mphambu, akakhala wamwamuna, umuyesere wa masekeli khumi ndi asanu, akakhala wamkazi wa masekeli khumi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Akakhala munthu wa zaka makumi asanu ndi limodzi ndi mphambu, akakhala wamwamuna, umuyesere wa masekeli khumi ndi asanu, akakhala wamkazi wa masekeli khumi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Munthu wake akakhala wa zaka 60 kapena kupitirirapo, mtengo wake ukhale wokwana masekeli asiliva 15 pa munthu wamwamuna, ndipo khumi pa munthu wamkazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ngati ndi munthu wa zaka makumi asanu ndi limodzi kapena kuposerapo, mtengo wa wamwamuna ukhale masekeli khumi ndi asanu, ndipo wamkazi ukhale masekeli khumi. Onani mutuwo |