Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 27:24 - Buku Lopatulika

24 Chaka choliza lipenga mundawo ubwerere kwa iye amene adaugulitsa, kwa iye amene dzikoli ndi lakelake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Chaka choliza lipenga mundawo ubwerere kwa iye amene adaugulitsa, kwa iye amene dzikoli ndi lakelake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Pa chaka chokondwerera zaka 50, mundawo udzabwezedwa kwa munthu amene adaugulitsayo, amene mtundawo unali wake ngati choloŵa chake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Pa chaka chokondwerera zaka makumi asanu, mundawo udzabwezedwa kwa munthu amene anawugulitsayo, amene malowo anali ake.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 27:24
5 Mawu Ofanana  

Chaka choliza lipenga ichi mubwerere nonse ku zakezake.


Koma dzanja lake likapanda kupeza zofikira za kumbwezera, pamenepo chogulitsacho chikhale m'dzanja lake la iye adachigulayo, kufikira chaka choliza lipenga; koma chaka choliza lipenga chituluke, nabwerere iye ku dziko lake.


Koma akapanda kuombola mundawo, kapena atagulitsa mundawo kwa munthu wina, suomboledwanso;


pamenepo wansembeyo amwerengere mtengo wake wa kuyesa kwako kufikira chaka choliza lipenga; ndipo apereke kuyesa kwako tsiku lomwelo, chikhale chinthu chopatulikira Yehova.


Ndipo kuyesa kwako konse kukhale monga mwa sekeli wa malo opatulika sekeli ndi magera makumi awiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa