Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 27:23 - Buku Lopatulika

23 pamenepo wansembeyo amwerengere mtengo wake wa kuyesa kwako kufikira chaka choliza lipenga; ndipo apereke kuyesa kwako tsiku lomwelo, chikhale chinthu chopatulikira Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 pamenepo wansembeyo amwerengere mtengo wake wa kuyesa kwako kufikira chaka choliza lipenga; ndipo apereke kuyesa kwako tsiku lomwelo, chikhale chinthu chopatulikira Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 wansembe aŵerenge mtengo wake kufikira pa chaka chokondwerera zaka 50. Tsono munthuyo apereke ndalama zokwanira mtengo wake pa tsikulo, kuti zikhale zopatulikira Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 wansembe atchule mtengo wake kufikira pa chaka chokondwerera zaka makumi asanu, ndipo munthuyo apereke ndalama zokwanira mtengo wake pa tsikulo monga ndalama zopatulika kwa Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 27:23
4 Mawu Ofanana  

ndipo wansembeyo aiyese mtengo wake, ingakhale yokoma kapena yoipa; monga uiyesa wansembewe, momwemo.


Akaupatula munda wake chitapita chaka choliza lipenga, wansembe azimwerengera ndalama monga mwa zaka zotsalira kufikira chaka choliza lipenga, nazichepsako pa kuyesa kwako.


Ndipo akapatulira Yehova munda woti adaugula, wosati wogawako ku munda wakewake;


Chaka choliza lipenga mundawo ubwerere kwa iye amene adaugulitsa, kwa iye amene dzikoli ndi lakelake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa